Job 35:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
inu aYobe mumangolankhula zopandapake, mukungochulukitsa mau opanda nzeru.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
chifukwa chake Yobu anatsegula pakamwa pake mwachabe, nachulukitsa mau opanda nzeru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
abambo Yobu mumangoyankhula zopandapake, mukungochulukitsa mawu opanda nzeru.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace Yobu anatsegula pakamwa pace mwacabe, Nacurukitsa mau opanda nzeru.