Job 35:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzakuyankhani inuyo ndi abwenzi anu omwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndidzakuyankhani, ndi anzanu pamodzi ndi inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ine ndikufuna ndikuyankheni inu pamodzi ndi abwenzi anu omwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndidzakuyankhani, Ndi anzanu pamodzi ndi inu.