Job 37:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mpweya wa Mulungu umaunditsa chisanu, ndipo madzi am'nyanja amauma kuti gwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwa kupuma kwake Mulungu apereka chipale, ndi madzi achitando aundana.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mpweya wa Mulungu umawunditsa madzi ndipo madzi a mʼnyanja amawuma kuti gwaa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwa kupuma kwace apereka cipale, Ndi madzi acitando aundana.