Job 38:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono ndidati, ‘Ufike mpaka apo osabzolapo, mafunde ako amphamvuwo aime pomwepo.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi kuti, Ufike mpaka apa, osapitirirapo; apa adzaletseka mafunde ako odzikuza?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene ndinati, ‘Ufike mpaka apa ndipo usapitirire apa ndiye pamene mafunde ako amphamvuwo azilekezera?’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi kuti, Ufike mpaka apa, osapitirirapo; Apa adzaletseka mafunde ako odzikuza?