Job 38:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi chibadwire chako udalamulapo dzuŵa kuti lituluke m'maŵa, ndi kuti mbandakucha ukhalepo pa nthaŵi yake?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi walamulira m'mawa chiyambire masiku ako, ndi kudziwitsa mbandakucha malo ake;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi chibadwire chako unalamulapo dzuwa kuti lituluke mmawa, kapena kuti mʼbandakucha ukhalepo pa nthawi yake,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi walamulira m'mawa ciyambire masiku ako, Ndi kudziwitsa mbanda kuca malo ace;