Job 38:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi iweyo udalamulapo kuti kuŵala kwa mbandakuchawo kuunikire dziko lonse lapansi, kuti kuthaŵitse anthu oipa obisala pamenepo?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti agwire malekezero a dziko lapansi, nakutumule oipa achokeko?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuti kuwalako kuwunikire dziko lonse lapansi ndi kuthamangitsa anthu oyipa?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kuti agwire malekezero a dziko lapansi, Nakutumule oipa acokeko?