Job 38:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuŵala kwa dzuŵa sikuŵafika anthu oipa, choncho sangathe kugwira ntchito zao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi kuunika kwa oipa kuletsedwa kuti asakuone, ndi dzanja losamulidwa lithyoledwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuwala kwa dzuwako sikuwafikira anthu oyipa, ndipo dzanja lawo silingathe kuchita kanthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi kuunika kwa oipa kuletsedwa kuti asakuone, Ndi dzanja losamulidwa lityoledwa.