Job 38:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi adakuwonetsa iwe zipata za imfa? Kodi udaonako ku dziko la anthu akufa kumene kuli mdima wokhawokha?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi zipata za imfa zinavumbulukira iwe? Kapena kodi unaona zipata za mthunzi wa imfa?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi anakuonetsapo zipata za imfa? Kodi unaonako ku dziko la anthu akufa kumene kuli mdima wandiweyani?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi zipata za imfa zinabvumbulukira iwe? Kapena kodi unaona zipata za mthunzi wa imfa?