Job 38:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi kukula kwa dziko lapansi umakudziŵa? Undiwuze tsono ngati umazidziŵa zonsezi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi unazindikira chitando cha dziko lapansi? Fotokozera, ngati uchidziwa chonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi kukula kwa dziko lapansi umakudziwa? Undiwuze ngati ukuzidziwa zonsezi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi unazindikira citando ca dziko lapansi? Fotokozera, ngati ucidziwa conse.