Job 38:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi njira yopita kumene kumakhala kuŵala ili kuti? Nanga mdima, kwao nkuti?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ili kuti njira yomukira pokhala kuunika? Ndi mdima, pokhala pake pali kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi njira yopita kumene kumakhala kuwala ili kuti? Nanga mdima umakhala kuti?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iri kuti njira yomukira pokhala kuunika? Ndi mdima, pokhala pace pali kuti,