Job 38:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi iwe ungathe kuziperekeza kwaoko zimenezi, kodi ukuidziŵa njira yopita kwaoko?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti upite nao kumalire ake, kuti uzindikire miseu ya kunyumba yake?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi iwe ungathe kuziperekeza kwawoko zimenezi? Kodi ukuyidziwa njira yopita kwawoko?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kuti upite nao ku malire ace, Kuti uzindikire miseu ya ku nyumba yace?