Job 38:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Makamaka ukudziŵadi ati, poti paja nthaŵi imeneyo nkuti iweyo utabadwa, ndipo zaka zako kuchuluka ati!
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Udziwa, pakuti unabadwa pamenepo, ndi masiku ako achuluka kuwerenga kwao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndithu, iwe ukuyidziwa, poti paja nthawi imeneyo nʼkuti utabadwa kale! Wakhala ndi moyo zaka zambiridi!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Udziwa, pakuti unabadwa pamenepo, Ndi masiku ako acuruka kuwerenga kwao.