Job 38:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zimenezi ndazisungira nthaŵi ya mavuto, ndidzazitumiza nthaŵi yomenyana nkhondo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
amene ndiwasungira tsiku la nsautso, tsiku lakulimbana nkhondo?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
zimene ndazisungira nthawi ya mavuto ndi nthawi yomenyana ndi ya nkhondo?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Amene ndiwasungira tsiku la nsautso, Tsiku lakulimbana nkhondo?