Job 38:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi udapitako kumene kumatulukira dzuŵa, kapena kumene kumachokera mphepo yakuvuma?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Njira ili kuti yomukira pogawikana kuunika, kapena pomwazikira mphepo ya kum'mawa pa dziko lapansi?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi umadziwa njira ya kumene kumachokera chingʼaningʼani kapena njira ya kumene kumachokera mphepo ya kummawa imene ili pa dziko lonse lapansi?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Njira iri kuti yomukira pogawikana kuunika, Kapena pomwazikira mphepo ya kum'mawa pa dziko lapansi?