Job 38:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi ndani amene adakonza ngalande za mvula? Ndani adakonza njira zodzeramo mphezi?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndani anachikumbira mchera chimvula, kapena njira ya bingu la mphezi,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi ndani amene amakonza ngalande za mvula, nanga ndani anakonza njira yoyendamo mphenzi,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndani anacikumbira mcera cimvula, Kapena njira ya bingu la mphezi,