Job 38:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndani amathirira dziko louma lagwaa, kotero kuti udzu umamerapo?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kukhutitsa thengo la kunkhwangwala, ndi kuphukitsa msipu?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kukhutitsa nthaka yowuma yagwaa ndi kumeretsamo udzu?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kukhutitsa thengo la kunkhwangwala, Ndi kuphukitsa msipu?