Job 38:28 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi mvula ili ndi bambo wake? Nanga madzi a mame adaŵabeleka ndani?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi mvula ili naye atate? Kapena wabala ndani madontho a mame?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi mvula ili ndi abambo ake? Nanga madzi a mame anawabereka ndani?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi mvula iri naye atate? Kapena wabala ndani madontho amame?