Job 38:30 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndani amasandutsa madzi kuti alimbe ngati mwala, pamene madzi apanyanja amazizira, nalimba kuti gwaa?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Madzi aundana ngati mwala, ndi pamwamba pa nyanja yozama mpogwirana madzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pamene madzi amawuma gwaa ngati mwala, pamene madzi a pa nyanja amazizira, nalimba kuti gwaa?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Madzi aundana ngati mwala, Ndi pamwamba pa nyanja yozama mpogwirana madzi.