Job 38:31 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi Nsangwe iwe ungazimange maunyolo? Kodi zingwe za Akamwiniatsatana iwe ungathe kuzimasula?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi ungamange gulu la Nsangwe? Kapena kumasula zomangira za Akamwiniatsatana?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi iwe ungayimitse kuyenda kwa nyenyezi? Kodi ungathe kuletsa kuyenda kwa nsangwe ndi akamwiniatsatana?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi ungamange gulu la Nsangwe? Kapena kumasula zomangira za Akamwiniatsatana?