Job 38:33 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi malamulo a mlengalenga umaŵadziŵa? Nanga ulamuliro wake, kodi ungaukhazikitse pa dziko lapansi?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi udziwa malemba a kuthambo? Ukhoza kukhazikitsa ufumu wao pa dziko lapansi?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi malamulo a mlengalenga umawadziwa? Kodi ungathe kukhazikitsa ulamuliro wa Mulungu pa dziko lapansi?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi udziwa malemba a kuthambo? Ukhoza kukhazikitsa ufumu wao pa dziko lapansi?