Job 38:34 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi iwe ungathe kulamula mitambo kuti igwetse mvula ya chigumula?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi udziwa kukwezera mau ako kumitambo, kuti madzi ochuluka akukute?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi iwe ungathe kulamula mitambo kuti igwetse mvula ya chigumula?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi udziwa kukwezera mau ako kumitambo, Kuti madzi ocuruka akukute?