Job 38:35 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi ungathe kutumiza zing'aning'ani kuti zing'anipe, ndi kugwera pa malo amene iwe ukufuna?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi ukhoza kutumiza mphezi kuti zimuke, ndi kunena nawe, Tili pano?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi ungathe kutumiza zingʼaningʼani kuti zingʼanime? Kodi zimabwera pamaso pako ndi kuti, ‘Tili pano?’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi ukhoza kutumiza mphezi kuti zimuke, Ndi kunena nawe, Tiri pano?