Job 38:36 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndani amene adayala mitambo bwino mu mlengalenga? Nanga ndani adalangiza mvula kuti igwere pakutipakuti?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndani analonga nzeru m'mitambomo? Ndani waninkha nyenyezi yotsotsoka luntha?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi ndani anayika nzeru mu mtima, ndani analonga mʼmaganizo nzeru zomvetsa zinthu?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndani analonga nzeru m'mitambomo? Ndani waninkha nyenyezi yotsotsoka luntha?