Job 38:37 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wanzeru ndani amene angathe kuŵerenga mitambo, nanga ndani angathe kupendeketsa mitsuko ya madzi akuthambo
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Adziwa ndani kuwerenga mitambo mwanzeru, ndi kutsanulira michenje ya kuthambo ndani,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Wanzeru ndani amene angathe kuwerenga mitambo? Ndani angathe kupendeketsa mitsuko ya madzi akuthambo
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Adziwa ndani kuwerenga mitambo mwanzeru, Ndi kutsanulira micenje ya kuthambo ndani,