Job 38:39 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi iwe ungathe kuufunira chakudya mkango? Kodi ungathe kuipatsa chakudya misona yake ija,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi ukhoza kusakira mkango waukazi nyama? Ndi kukwaniritsa chakudya cha misona,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi ndani amawusakira chakudya mkango waukazi ndi kukhutitsa misona ya mikango
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi ukhoza kusakira mkango waukazi nyama? Ndi kukwaniritsa cakudya ca misona,