Job 38:40 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
pamene ili khale m'mapanga mwake, kapena pamene ikubisala m'tchire?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pamene ibwatama m'ngaka mwao, nikhala mobisala kulaliramo?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pamene ili khale mʼmapanga mwawo kapena pamene ikubisala pa tchire?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamene ibwathama m'ngaka mwao, Nikhala mobisala kulaliramo?