Job 38:41 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi khwangwala amampatsa chakudya chake ndani, pamene maunda ake akulirira kwa Mulungu, namadzandira chifukwa chosoŵa chakudya?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Amkonzeratu khungubwi chakudya chake ndani, pamenepo ana ake afuulira kwa Mulungu, naulukauluka osowa chakudya?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi amamupatsa khwangwala chakudya chake ndani pamene ana ake akulirira kwa Mulungu ndi kumayendayenda chifukwa chosowa zakudya?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Amkonzeratu khungubwi cakudya cace ndani, Pamene ana ace apfuulira kwa Mulungu, Nauluka-uluka osowa cakudya?