Job 38:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi maziko ake adaŵakumba potani? Nanga mwala wake wapangodya adauika ndani?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maziko ake anakumbidwa pa chiyani? Kapena anaika ndani mwala wake wa pangodya,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi maziko ake anawakumba potani, kapena ndani anayika mwala wake wapangodya,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maziko ace anakumbidwa pa ciani? Kapena anaika ndani mwala wace wa pangondya,