Job 38:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi ndani amene adatsekera nyanja pamene inkalengedwa pamene inkachita ngati kutumphuka pansi pa dziko?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kapena anatseka nyanja ndani ndi zitseko, muja idakamula ngati kutuluka m'mimba,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi ndani amene anatsekera nyanja pamene inkalengedwa, pamene inkachita ngati kutumphuka pansi pa dziko,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kapena anatseka nyanja ndani ndi zitseko, Muja idakamula ngati kuturuka m'mimba,