Job 38:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndinetu amene ndidakuta nyanjayo ndi mitambo, ndidaiveka mdima ngati chovala.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
muja ndinayesa mtambo chovala chake, ndi mdima wa bii nsalu yake yokulunga,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pamene ndinasandutsa mitambo kukhala chovala chake ndi kuyikulunga mu mdima wandiweyani,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Muja ndinayesa mtambo cobvala cace, Ndi mdima wa bii nsaru yace yakulunga,