Job 39:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi ungakhulupirire kuti idzabwera nkudzatuta tirigu wako ku malo opunthira?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi udzaitama kuti itute mbeu zako, ndi kuzisonkhanitsira kudwale?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi ungadalire kuti idzakubweretsera tirigu wako ndi kumuyika ku malo opunthira?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi udzaitama kuti itute mbeu zako, Ndi kuzisonkhanitsira kudwale?