Job 39:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nthiŵatiŵa imafotsera mazira ake pansi, kuti afundidwe m'nthaka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti isiya mazira ake panthaka, nimafunditsa m'fumbi,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nthiwatiwa imakwirira mazira ake pansi ndipo amafundidwa ndi nthaka,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti isiya mazira ace panthaka, Nimafunditsa m'pfumbi,