Job 39:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja Mulungu adaimana nzeru, kotero kuti simvetsa kanthu kalikonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti Mulungu anaimana nzeru, ndipo sanaigawire luntha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chifukwa Mulungu anayimana nzeru, simvetsa kanthu kalikonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Mulungu anaimana nzeru, Ndipo sanaigawira luntha.