Job 39:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi ndi nzeru zako zimene zimaphunzitsa kabaŵi kuuluka, ndi kutambalitsa mapiko ake kupita chakumwera?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi kabawi auluka mwa nzeru zako, natambasula mapiko ake kunka kumwera?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi kabawi amawuluka ndi nzeru zako, ndi kutambasula mapiko ake kupita kummwera?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi kabawi auluka mwa nzeru zako, Natambasula mapiko ace kumka kumwera?