Job 39:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi ukuidziŵa nthaŵi imene zidzakhala tsonga nkuswa ana, kenaka nkutayiza?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zithuntha, ziswa, zitaya zowawa zao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zimakhala tsonga ndi kuswa ana awo; pamenepo ululu wobereka nʼkutha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zithuntha, ziswa, Zitaya zowawa zao.