Job 40:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ine sindili kanthu konse! Kodi ndingathe kukuyankhani chiyani? Palibe, koma kungogwira pakamwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, ndakhululuka ine, ndidzakubwezerani mau otani? Ndigwira pakamwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ine sindili kanthu konse, kodi ndingathe kukuyankhani chiyani? Ndagwira pakamwa panga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, ndakhululuka ine, ndidzakubwezerani mau otani? Ndigwira pakamwa.