Job 40:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi uli ndi mphamvu monga Ine Mulungu? Kodi mau ako angagunde monga m'mene amagundira mau anga?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi uli nalo dzanja ngati Ine Mulungu? Kapena ukhoza kugunda ndi mau ngati Ine?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi uli ndi dzanja monga la Mulungu, ndipo mawu ako angagunde ngati mphenzi monga a Mulungu?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi uli nalo dzanja ngati Ine Mulungu? Kapena ukhoza kugunda ndi mau ngati Ine?