Job 41:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati palibe wina woti angalimbe mtima nkuchiputa. Nanga ndani angalimbe mtima nkukangana ndi Ine Mulungu?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Palibe wolimba mtima kuti adzaiputa. Ndipo ndaniyo adzaima pamaso pa Ine?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Palibe wolimba mtima kuti ndi kuyiputa. Ndani angalimbe mtima kulimbana ndi Ine?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Palibe wolimba mtima kuti adzaiputa. Ndipo ndaniyo adzaima pamaso pa Ine?