Job 41:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kumsana kwake kuli mizere ya mamba onga zishango zolumikizanalumikizana, onse olimba ngati mwala.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mamba ake olimba ndiwo kudzitama kwake; amangika pamodzi ngati okomeredwatu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kumsana kwake kuli mizere ya mamba onga zishango zolumikizanalumikizana;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maamba ace olimba ndiwo kudzitama kwace; Amangika pamodzi ngati okomeredwatu.