Job 41:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pachifuwa pake mpouma ngati mwala. Pali gwa! Ngati mwala wa mphero.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wake ulimba ngati mwala, inde ulimba ngati mwala wa mphero.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pachifuwa pake ndi powuma ngati mwala, ndi pa gwaa, ngati mwala wamphero.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wace ulimba ngati mwala, Inde ulimba ngati mwala wa mphero,