Job 41:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zibonga zimakhala ngati ziputu. Akamachitchaya ndi nthungo, icho chimangoseka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zibonga ziyesedwa chiputu, iseka kuthikuza kwake kwa nthungo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zibonga zimakhala ngati ziputu; imangoseka pamene akuyibaya ndi nthungo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zibonga ziyesedwa ciputu, Iseka kuthikuza kwace kwa nthungo,