Job 41:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi chidzachita nawe chipangano kuti chikhale chokutumikira mpaka muyaya?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi idzapangana ndi iwe, kuti uitenge ikhale kapolo wako wachikhalire?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi idzachita nawe mgwirizano kuti uyisandutse kapolo wako mpaka muyaya?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi idzapangana ndi iwe, Kuti uitenge ikhale kapolo wako wacikhalire?