Job 42:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adabalanso ana aamuna asanu ndi aŵiri ndi ana aakazi atatu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anali naonso ana amuna asanu ndi awiri ndi ana akazi atatu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anaberekanso ana aamuna asanu ndi awiri ndi ana aakazi atatu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anali naonso ana amuna asanu ndi awiri ndi ana akazi atatu.