Job 42:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ndikudziŵa kuti Inu mungathe kuchita zinthu zonse, chimene mufuna kuchita, wina sangaletse konse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndidziwa kuti mukhoza kuchita zonse, ndi kuti palibe choletsa cholingirira chanu chilichonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ndikudziwa kuti Inu mungathe kuchita zinthu zonse; chimene mufuna kuchita wina sangaletse konse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndidziwa kuti mukhoza kucita zonse, Ndi kuti palibe coletsa colingirira canu ciri conse,