Job 5:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Iwe Yobe, itana tsono. Kodi alipo wina aliyense adzakuyankhe? Kodi ndi kwa mngelo uti ungapeze thandizo?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Itana tsono; pali wina wakukuyankha kodi? Ndipo udzatembenukira kwa yani wa oyera mtimawo?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Itana ngati ungathe, koma ndani adzakuyankhe? Kodi ndi kwa mngelo uti ungapezeko thandizo?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Itana tsono; pali wina wakukuyankha kodi? Ndipo udzatembenukira kwa yani wa oyera mtimawo?