Job 5:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho amphaŵi amaŵalimbitsa mtima, koma anthu oipa amaŵatseka pakamwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Potero aumphawi ali nacho chiyembekezo, ndi mphulupulu yatsekedwa pakamwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho osauka ali ndi chiyembekezo, ndipo anthu opanda chilungamo amawatseka pakamwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Potero aumphawi ali naco ciyembekezo, Ndi mphulupulu yatsekedwa pakamwa.