Job 5:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakuti ndiye amene amavulaza namangaponso mabala. Amakantha, komanso manja ake amachiritsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti apweteka, namanganso mabala; alasa, ndi manja ake omwe apoletsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti Iye amavulaza koma amamanganso mabalawo; Iye amakantha munthu, komanso manja ake amachiritsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti apweteka, namanganso mabala; Alasa, ndi manja ace omwe apoletsa.