Job 5:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Udzafika ku manda utakalamba, monga m'mene zokolola zimachera pa nyengo yake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Udzafika kumanda utakalamba, monga abwera nao mtolo wa tirigu m'nyengo yake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Udzafika ku manda utakalamba, monga mitolo ya zokolola pa nyengo yake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Udzafika kumanda utakalamba, Monga abwera nao mtolo wa tirigu m'nyengo yace.