Job 6:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zimenezi zikadandisangalatsa, ndikadakondwa nazo kwambiri ngakhale zipweteke chotani, podziŵa kuti sindidakane mau a Woyera uja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo ndidzasangalala, ndidzakondwera nacho chowawa chosandileka; pakuti sindinawabisa mau a Woyerayo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo ine ndikanakhalabe ndi chitonthozo ichi, ndikanakondwa mu ululu wanga wosalekezawu podziwa kuti sindinakane mawu a Woyerayo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo ndidzasangalala, Ndidzakondwera naco cowawa cosandileka; Pakuti sindinawabisa mau a Woyerayo.