Job 6:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi mphamvu zanga ndi zotani kuti ndizikhalabe ndi moyo? Nanga moyo wanga ukupitiriranji, ngati chiyembekezo palibe?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mphamvu yanga njotani kuti ndiyembekeze? Mathedwe anga ndi otani kuti ndipirire?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi mphamvu zanga nʼzotani kuti ndizikhalabe ndi chiyembekezo? Nanga zoyembekezera zanga nʼzotani kuti ndipirirebe?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mphamvu yanga njotani kuti ndiyembekeze? Mathedwe anga ndi otani kuti ndipirire?